1
GENESIS 18:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.
مقایسه
GENESIS 18:14 را جستجو کنید
2
GENESIS 18:12
ndipo Sara anaseka m'mtima mwake, nati, Kodi ndidzakhala ndi kukondwa ine nditakalamba, ndiponso mbuyanga ali wokalamba?
GENESIS 18:12 را جستجو کنید
3
GENESIS 18:18
Pakuti Abrahamu adzakhala ndithu wamkulu ndi wamphamvu, ndipo mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsika mwa iye?
GENESIS 18:18 را جستجو کنید
4
GENESIS 18:23-24
Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Kapena alipo olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi; kodi mudzaononga, simudzasiya malowo chifukwa cha olungama makumi asanu ali momwemo?
GENESIS 18:23-24 را جستجو کنید
5
GENESIS 18:26
Ndipo anati Yehova, Ndikapeza m'Sodomu olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi, ndidzasiya malo onse chifukwa cha iwo.
GENESIS 18:26 را جستجو کنید
خانه
كتابمقدس
برنامههای مطالعه
ویدیوها