YouVersionロゴ
聖書読書プランビデオ
アプリを入手
言語選択
検索アイコン

YOHANE 5の有名な聖句

1

YOHANE 5:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Indetu, indetu, ndinena kwa inu, kuti iye wakumva mau anga, ndi kukhulupirira Iye amene anandituma Ine, ali nao moyo wosatha, ndipo salowa m'kuweruza, koma wachokera kuimfa, nalowa m'moyo.

比較

YOHANE 5:24で検索

2

YOHANE 5:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu, pakuona ameneyo alikugona, ndipo anadziwa kuti anatero nthawi yaikulu pamenepo, ananena naye, Ufuna kuchiritsidwa kodi?

比較

YOHANE 5:6で検索

3

YOHANE 5:39-40

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo; ndipo simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo.

比較

YOHANE 5:39-40で検索

4

YOHANE 5:8-9

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu ananena naye, Tauka, yalula mphasa yako, nuyende. Ndipo pomwepo munthuyu anachira, nayalula mphasa yake, nayenda. Koma tsiku lomwelo linali la Sabata.

比較

YOHANE 5:8-9で検索

5

YOHANE 5:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pamenepo Yesu anayankha nati kwa iwo, Indetu, indetu ndinena kwa inu, sakhoza Mwana kuchita kanthu pa yekha, koma chimene aona Atate achichita, ndicho. Pakuti zimene Iye azichita, zomwezo Mwananso azichita momwemo.

比較

YOHANE 5:19で検索

無料の読書プランとYOHANE 5に関係したデボーション

前章
次章
YouVersion

日々、神との親しい交わりを求めるために、あなたを励まし、勇気を与えます。

ミニストリー

概要

キャリア

ボランティア

ブログ

プレス

便利なリンク集

ヘルプ

寄付

聖書の訳

オーディオ聖書

聖書の言語

今日の聖句


デジタルミニストリー

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

プライバシー規約利用規約
脆弱性の開示
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

ホーム

聖書

読書プラン

ビデオ