Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

LUKA 1:35

LUKA 1:35 BLPB2014

Ndipo mngelo anayankha, nati kwa iye, Mzimu Woyera adzafika pa iwe, ndi mphamvu ya Wamkulukulu idzakuphimba iwe: chifukwa chakenso Choyeracho chikadzabadwa, chidzatchedwa Mwana wa Mulungu.