1
Genesis 11:6-7
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Yehova anati, “Anthuwa ndi amodzi, ndipo ali ndi chiyankhulo chimodzi. Izi akuchitazi nʼchiyambi chabe cha zomwe akufuna kukwaniritsa kuchita. Tiyeni titsikireko tikasokoneze chiyankhulo chawo kuti asamamvetsetsane.”
موازنہ
تلاش Genesis 11:6-7
2
Genesis 11:4
Kenaka anati, “Tiyeni tidzimangire mzinda wokhala ndi nsanja yoti ikafike kumwamba kuti titchuke. Kupanda kutero tibalalikana pa dziko lonse lapansi.”
تلاش Genesis 11:4
3
Genesis 11:9
Nʼchifukwa chake mzindawo unatchedwa Babeli, popeza Yehova anasokoneza chiyankhulo cha anthu onse. Powachotsa kumeneko, Yehova anawabalalitsira pa dziko lonse lapansi.
تلاش Genesis 11:9
4
Genesis 11:1
Nthawi imeneyo anthu onse a pa dziko lapansi ankayankhula chiyankhulo chimodzi ndipo mawu amene ankayankhula anali amodzi.
تلاش Genesis 11:1
5
Genesis 11:5
Koma Yehova anatsika kudzaona mzindawo ndi nsanja imene anthu aja ankayimanga.
تلاش Genesis 11:5
6
Genesis 11:8
Choncho Yehova anabalalitsa anthu aja pa dziko lonse lapansi ndipo analeka kumanga mzindawo.
تلاش Genesis 11:8
صفحہ اول
بائبل
مطالعاتی منصوبہ
Videos