YouVersion Logo
بائبلمطالعاتی منصوبہVideos
اپلی کیشن حاصل کریں
زبان کا انتخاب کنندہ
تلاش

GENESIS 2 سے مشہور بائبلی آیات

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

موازنہ

تلاش GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

موازنہ

تلاش GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

موازنہ

تلاش GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

موازنہ

تلاش GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

موازنہ

تلاش GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

موازنہ

تلاش GENESIS 2:25

پچھلا باب
اگلا باب
YouVersion

آپ کو ہر روز خدا کے ساتھ قربت حاصل کرنے کی ترغیب دینا اور چیلنج کرنا۔.

خدمت

بارے میں

آسامیاں

رضاکار

Blog

Press

Useful Links

مدد

ہدیہ دیں

بائبل ورژن

Audio Bibles

بائبل کی زبانیں

آج کی آیت


کی ایک ڈیجیٹل خدمت

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Privacy Policyشرائط
حساس کا انکشاف کرنے والا عمل
FacebookTwitterInstagramیوٹیوبپنٹیرسٹ

صفحہ اول

بائبل

مطالعاتی منصوبہ

Videos