YouVersion Logo
بائبلمطالعاتی منصوبہVideos
اپلی کیشن حاصل کریں
زبان کا انتخاب کنندہ
تلاش

GENESIS 7 سے مشہور بائبلی آیات

1

GENESIS 7:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

موازنہ

تلاش GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

موازنہ

تلاش GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

موازنہ

تلاش GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

موازنہ

تلاش GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

موازنہ

تلاش GENESIS 7:12

پچھلا باب
اگلا باب
YouVersion

آپ کو ہر روز خدا کے ساتھ قربت حاصل کرنے کی ترغیب دینا اور چیلنج کرنا۔.

خدمت

بارے میں

آسامیاں

رضاکار

Blog

Press

Useful Links

مدد

ہدیہ دیں

بائبل ورژن

Audio Bibles

بائبل کی زبانیں

آج کی آیت


کی ایک ڈیجیٹل خدمت

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Privacy Policyشرائط
حساس کا انکشاف کرنے والا عمل
FacebookTwitterInstagramیوٹیوبپنٹیرسٹ

صفحہ اول

بائبل

مطالعاتی منصوبہ

Videos