1
LUKA 23:34
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere.
Lee anya n'etiti ihe abụọ
Nyochaa LUKA 23:34
2
LUKA 23:43
Ndipo Iye ananena naye, Indetu, ndinena ndi iwe, Lero lino udzakhala ndine m'Paradaiso.
Nyochaa LUKA 23:43
3
LUKA 23:42
Ndipo ananena, Yesu, ndikumbukireni m'mene mulowa Ufumu wanu.
Nyochaa LUKA 23:42
4
LUKA 23:46
Ndipo pamene Yesu anafuula ndi mau akulu, anati, Atate, m'manja mwanu ndipereka mzimu wanga. Ndipo pakutero anapereka mzimu wake.
Nyochaa LUKA 23:46
5
LUKA 23:33
Ndipo pamene anafika kumalo dzina lake Bade, anampachika Iye pamtanda pomwepo, ndi ochita zoipa omwe, mmodzi kudzanja lamanja ndi wina kulamanzere.
Nyochaa LUKA 23:33
6
LUKA 23:44-45
Ndipo ora lake pamenepo linali ngati lachisanu ndi chimodzi. Ndipo panali mdima pa dziko lonse kufikira ora lachisanu ndi chinai, ndipo dzuwa linada. Ndipo nsalu yotchinga ya m'Kachisi inang'ambika pakati.
Nyochaa LUKA 23:44-45
7
LUKA 23:47
Ndipo pamene kenturiyo anaona chinachitikacho, analemekeza Mulungu, nanena, Zoonadi munthu uyu anali wolungama.
Nyochaa LUKA 23:47
Ebe Mmepe Nke Mbụ Nke Ngwá
Akwụkwọ Nsọ
Atụmatụ Ihe Ogụgụ Gasị
Vidiyo Gasị