YouVersion embleem
BybelLeesplanneVideo's
Kry die toep
Taalkieser
Soek-ikoon

Gewilde Bybelverse vanaf GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Vergelyk

Verken GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo anapambana madzi padziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Vergelyk

Verken GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Vergelyk

Verken GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali padziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa padziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Vergelyk

Verken GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo mvula inali padziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Vergelyk

Verken GENESIS 7:12

Vorige hoofstuk
Volgende hoofstuk
YouVersion

Moedig jou aan en daag jou uit om elke dag intimiteit met God op te soek.

Bediening

Iets oor ons

Loopbane

Vrywilliger

Webjoernaal

Media

Nuttige skakels

Hulp

Skenk

Bybelweergawes

Klankbybels

Bybeltale

Vers-van-die-dag


'n Digitale bediening van

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivaatheidsbeleidVoorwaardes
Program vir die openbaarmaking van kwesbaarheid
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Tuisblad

Bybel

Leesplanne

Video's