1
LUKA 21:36
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Koma inu dikirani nyengo zonse, ndi kupemphera, kuti mukalimbike kupulumuka zonse zimene zidzachitika, ndi kuimirira pamaso pa Mwana wa Munthu.
సరిపోల్చండి
LUKA 21:36 ని అన్వేషించండి
2
LUKA 21:34
Koma mudziyang'anire nokha, kuti kapena mitima yanu ingalemetsedwe ndi madyaidya ndi kuledzera, ndi zosamalira za moyo uno, ndi kuti tsiku ilo lingafikire inu modzidzimutsa ngati msampha
LUKA 21:34 ని అన్వేషించండి
3
LUKA 21:19
Mudzakhala nao moyo wanu m'chipiriro.
LUKA 21:19 ని అన్వేషించండి
4
LUKA 21:15
Pakuti Ine ndidzakupatsani inu kamwa ndi nzeru, zimene adani anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa.
LUKA 21:15 ని అన్వేషించండి
5
LUKA 21:33
Kumwamba ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.
LUKA 21:33 ని అన్వేషించండి
6
LUKA 21:25-27
Ndipo kudzakhala zizindikiro pa dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi; ndi pa dziko lapansi chisauko cha mitundu ya anthu, alikuthedwa nzeru pa mkukumo wake wa nyanja ndi mafunde ake; anthu akukomoka ndi mantha, ndi kuyembekezera zinthu zilinkudza kudziko lapansi; pakuti mphamvu zakumwamba zidzagwedezeka. Ndipo pamenepo adzaona Mwana wa Munthu alinkudza mu mtambo ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu.
LUKA 21:25-27 ని అన్వేషించండి
7
LUKA 21:17
Ndipo anthu onse adzadana ndi inu chifukwa cha dzina langa.
LUKA 21:17 ని అన్వేషించండి
8
LUKA 21:11
ndipo kudzakhala zivomezi zazikulu, ndi njala ndi miliri m'malo akutiakuti, ndipo kudzakhala zoopsa ndi zizindikiro zazikulu zakumwamba.
LUKA 21:11 ని అన్వేషించండి
9
LUKA 21:9-10
Ndipo pamene mudzamva za nkhondo ndi mapanduko, musaopsedwa; pakuti ziyenera izi ziyambe kuchitika; koma mathedwe sakhala pomwepo. Pamenepo ananena nao, Mtundu wa anthu udzaukira pa mtundu wina, ndipo ufumu pa ufumu wina
LUKA 21:9-10 ని అన్వేషించండి
10
LUKA 21:25-26
Ndipo kudzakhala zizindikiro pa dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi; ndi pa dziko lapansi chisauko cha mitundu ya anthu, alikuthedwa nzeru pa mkukumo wake wa nyanja ndi mafunde ake; anthu akukomoka ndi mantha, ndi kuyembekezera zinthu zilinkudza kudziko lapansi; pakuti mphamvu zakumwamba zidzagwedezeka.
LUKA 21:25-26 ని అన్వేషించండి
11
LUKA 21:10
Pamenepo ananena nao, Mtundu wa anthu udzaukira pa mtundu wina, ndipo ufumu pa ufumu wina
LUKA 21:10 ని అన్వేషించండి
12
LUKA 21:8
Ndipo Iye anati, Yang'anirani musasocheretsedwe; pakuti ambiri adzadza m'dzina langa, nadzanena, Ndine amene; ndipo, Nthawi yayandikira; musawatsate pambuyo pao.
LUKA 21:8 ని అన్వేషించండి
హోమ్
బైబిల్
ప్రణాళికలు
వీడియోలు